Wa security ku Parliament, Youngson Chilinde arrested

Wa security ku Parliament, Youngson Chilinde arrested

Published on June 2, 2013 at 7:54 AM by FACE OF MALAWI

44 words • approx. 1 min read

A Police ku Lilongwe akudziwitsa nonse kuti amanga officer wa security ku Parliament, Youngson Chilinde, kamba kosasantha makofu mtolankhani wa ku Nation Publications Limited, Thoko Banda.

Mtolankhani yu anamenyedwa makofu kumaso kufire ngati ngati waphoda magazi.

Youngson Chilinde akayankha mulandu wa Assault and battery

Subscribe to our Youtube Channel: