DR BANDA: My fellow
Malawians do you want
multiparty in Malawi? JOHN TEMBO : A malawi kodi
mukufuna matimati,kodi
mukufuna nkhondo?
——

Dr BANDA: some areas are
facing drought especially in the south.
TEMBO: madela ena
chakumwela uku ali ndi
drought.
——

DR BANDA: Where was Aleke Banda,Muluzi and his friends all
these years.?
TEMBO: kodi abongololo mudali
kuti nthawi
yonseyi,m’manjamo!:-) :-)

Subscribe to our Youtube Channel: