No featured image set for this post.

NACHIPANTI INCLUSIVE IN THE LIST OF 395 PARDONED PRISONERS.

Published on July 4, 2013 at 12:37 AM by FACE OF MALAWI

40 words • approx. 1 min read

Malingana ndi ma report omwe akungotipeza kumene, dzina la mnyamata uja osawutsa anthu pakuwayamwa magazi ndi kugona akazi ayeni Nachipanti, nalo lili pa n’ndandanda wa akayidi omwe president Banda waakhululukila pokondwelera kuti dziko la Malawi, lakwanitsa zaka 45 lili paufulu wozilamulira.

Subscribe to our Youtube Channel: