WAKUBA WAPHEDWA KU M’CHINJI!

WAKUBA WAPHEDWA KU M’CHINJI!

Published on July 15, 2013 at 5:45 PM by FACE OF MALAWI

40 words • approx. 1 min read

Patangodutsa masiku ochepa Pres. Joyce Banda atakhululukila bambo Maxwell Kapinga pachikondwelero choti dziko lino lakwanitsa zaka 49 lili pa ufulu wodzilamulira, bambowa dzulo akhaphidwa mpaka kuphedwa atawagwira akuba mbuzi m’khola la munthu wina m’bomali.

Omwe alanga wakubayu motere, sakudziwika mpaka pano.

Subscribe to our Youtube Channel: