2 pigeons per family

2 pigeons per family

Published on July 22, 2013 at 10:28 PM by FACE OF MALAWI

39 words • approx. 1 min read

President Joyce Banda wati tsopano ayamba kugawa ‘nkhunda’ kuti anthu adziweta pantchito yake yofuna kuthana ndi umphawi m’dziko muno. Malingana ndi Joyce, banja lomwe lizisankhidwa, lizilandila nkhunda ziwiri (yayimuna ndi yayikazi) ndipo programme yi idzitchedwa ‘2 pigeons per family’

Subscribe to our Youtube Channel: