A DPP A WOTCHA SUKULU YA JOYCE BANDA

A DPP A WOTCHA SUKULU YA JOYCE BANDA

Published on August 29, 2013 at 4:02 PM by FACE OF MALAWI

72 words • approx. 1 min read

Akuluakulu a chipani cholamula boma cha PP ati, sakupenekera konse kuti moto womwe watentha ma hostel anyamata pa sukulu ya Joyce Banda Foundation yaku Chimwankhunda ku Blantyre, anayatsa ndi a chipani cha DPP.

”ife sitikupenekera konse kapena kuchotsera kuti anachita zawupanduzi ndi achipani cha DPP chifukwa sakugona tulo ndi Mayi Joyce Banda. Akufunafuna njira zoti awagonjetse koma akulephera ndinkuwona achita izi. Koma ndiiiiiithu, anjatidwa posakhalitsa pamodzi ndi amene akuwatumayo” ayankhula chonchi mamulumuzanawa.

Subscribe to our Youtube Channel: