LYRICS OF DAVID KALIRANI’s SONG FEATURING BLACK FLAME ATTACKING PROPHET BUSHIRI

LYRICS OF DAVID KALIRANI’s SONG FEATURING BLACK FLAME ATTACKING PROPHET BUSHIRI

Published on March 31, 2016 at 3:28 PM by Robert Ngwira

258 words • approx. 2 min read

Who is this uncircumcised philistine?
Let’s call spade a spade, i dont beat
about
bush. Bushiri you are not a prophet /
U are not major yo majoring the
minus / kaguru kokusatiraka tikapanga
minus /
if they dont repent hellfire ah
go burn dem /
u need a light in your
ministry
The girls you are having sex
with are confirmation/ kuti utumiki
wako its an abomination /,,,
Akuti mphamvu zake amazitenga
kumadzi ,
mphamvu zako umazipeza through
divination /
Asing’anga ako akuyalutsa uli
mmadzi /
Kapinga tikutchetcha njoka zionekere /
Ndikumva ziwanda zako zikuti ”
Eeh ! papa game yalakwaapapa /
‘ UFITI ! ‘ / ndi ndikupukusa
legeni yanga kumwala/
Ndine mwana wa Mulungu
sungandiphe
ndimankhwala /
Blind followers please wear
spectacles /
And watch God making Bushiri a
public spectacle /
False prophets I will chop you down
Like Elijah and the prophets of baal /
Am ready to die on the battlefield,
God prepared me for this battle
kalekale /
Maybe u havent listened to
‘as u grow ‘ ‘ exodus part 2 “,
From experience I know God can kill
you
too /
Akuti ma prophet amene
timawatchula ma prophet ku Malawi
ndi anthu okuti apereka miyoyo yawo,
Apereka miyoyo ya anthu,
Sindiyisekelera mikangoyi,
Am ready to fight, mphamvu ya
Mzimu Oyera
Siyokuti mungochira kuthupi,
It’s not for u to get a car, wife, a new
house a
new house, it has been twisted /
Atembenuza purpose ya Mphamvu
Holy Spirit , they only prophecy about
material things / they are helping the
powers of darkness /
wayionankhondo ?
Anyambutimulikuti (osaopa)
Nthawiyankhondoiyi (osaopa)
Anenelionyengatithanenawo (osaopa)
Ufiti (osaopa)
Njoka (osaopa)
CLOSE DOWN YOUR
MINISTRIES ! THIS IS PART ONE !

Subscribe to our Youtube Channel: