Atupere Muluzi Sakubwera Poyera

Atupere Muluzi Sakubwera Poyera

Published on August 2, 2018 at 3:15 PM by Face of Malawi

56 words • approx. 1 min read

Mtsogoleri wa chipani cha United Democratic Front (UDF) Atupele Muluzi sakubwera poyera ngati adzapikisane nawo pa chisankho cha chaka chamawa.

Muluzi in the middle

Muluzi wakhala akugwira ntchito ndi boma m’maunduna osiyanasiyana kwa zaka zinayi potsatila m’gwilizano omwe chipani cha UDF chilli nawo ndi chipani cholamura cha DPP.

Subscribe to our Youtube Channel: