Veteran musician Joseph Nkasa has come out of his cocoon to release new hit single defending the Minister of Agriculture Irrigation and Water Development Dr. George Chaponda who is implicated in the maize-gate scandal, saying Chaponda’s hands are clean.

The hit single has attracted debate on the social media with others accusing Nkasa of trying to buy favours from the Minister.

In the song, Nkasa has described Malawians as traitors.

Below are the lyrics:

Nkhani ya George Chaponda ikundikumbutsa mwamuna wa m’Baibulo uja kale kale/Abale ake anamuda namuponya m’dzenje/ Napangana chiwembu…/Pofufuza chifukwa chomwe anawalakwira/ Sichinapezeke olo ngakhale pang’ono/ Ponena amati bwanji mwamuna ameneyu akuyanjana ndi bambo wathu kuposa tonse.

And the chorus goes:

Ndakulakwira chani mtundu wanga?
Mtima wako ukuwawa bwanji?
Inu mutamva ludzu/ Ndakupatsani madzi
Koma lero mwandimwetsa ndulu
Chimene mukufuna/Unduna wanga uthe/
Malawi’we
Ndiyankhe tsonoli
Chifundo chinaphetsa msema-mitondo/Ndiwolotse ndikakutafune
Mwandisandutsa wokuba
Nkhani ya chimanga
Mwaimitsa
Mboni zonama
Chimene ndachiwona
Mtima wanjiru, kaduka Nsanje
Zakula M’malawi
Inu mutamva ludzu
Ndakupatsani madzi
Koma lero
Mwandimwetsa ndulu

Subscribe to our Youtube Channel: